Ezekieli 21

Lupanga la Yehova 1 Ndipo anandidzera mau a Yehova, akuti, 2 Wobadwa ndi munthu iwe, lozetsa nkhope yako ku Yerusalemu, nuwabenthulire mau malo opatulikawa, nunenere dziko la Israyeli kulitsutsa; 3…

Ezekieli 22

Macimo oopsa a Yerusalemu 1 Anandidzeransomau a Yehova, akuti, 2 Ndipo iwe wobadwa ndi munthu, udzaweruza, udzauweruza mudziwo wa mwazi kodi? uudziwitse tsono zonyansa zace zonse. 3 Nuziti, Atero Ambuye…

Ezekieli 23

Ohola ndi Oholiba acigololowo 1 Ndipo anandidzera mau a Yehova, akuti, 2 Wobadwa ndi munthu iwe, panali akazi awiri, mai wao ndi mmodzi; 3 ndipo anacita cigololo iwo m’Aigupto, anacita…

Ezekieli 24

Fanizo la mphika wobwadamuka 1 Anandidzeranso mau a Yehova caka cacisanu ndi cinai, mwezi wakhumi, tsiku lakhumi la mwezi, ndi kuti, 2 Wobadwa ndi munthu iwe, Udzilembere dzina la tsiku…

Ezekieli 25

Aneneratu za kulangidwa kwa Aamoni 1 Ndipo mau a Yehova anandidzera, akuti, 2 Wobadwa ndi munthu iwe, Lozetsa nkhope yako kwa ana a Amoni, nuwanenere; 3 nunene kwa ana a…

Ezekieli 26

Za kulangidwa kwa Turo 1 Ndipo kunali caka cakhumi ndi cimodzi, tsiku loyamba la mwezi, anandidzera mau a Yehova, akuti, 2 Wobadwa ndi munthu iwe, popeza Turo ananyodola Yerusalemu, ndi…

Ezekieli 27

Nyimbo ya maliro ya pa Turo 1 Anandidzeranso mau a Yehova, akuti, 2 Ndipo iwe wobadwa ndi munthu, Takwezera Turo nyimbo ya maliro; 3 nuti kwa Turo, Iwe wakukhala polowera…

Ezekieli 28

Aneneratu za kulangidwa kwa mfumu ya ku Turo 1 Ndipo anandidzera mau a Yehova, akuti, 2 Wobadwa ndi munthu iwe, uziti kwa kalonga wa Turo, Atero Ambuye Yehova, Popeza mtima…

Ezekieli 29

Aneneratu za kulangidwa kwa Aigupto 1 Caka cakhumi, mwezi wakhumi, tsiku lakhumi ndi ciwiri la mweziwo, anandidzera mau a Yehova, akuti, 2 Wobadwa ndi munthu iwe, lozetsa: nkhope yako itsutsane…

Ezekieli 30

Aigupto adzagonjetsedwa ndi mfumu ya ku Babulo 1 Anandidzeranso mau a Yehova, akuti, 2 Wobadwa ndi munthu iwe, nenera, uziti, Atero Ambuye Yehova, Liritsani, Ha, tsikulo 3 Pakuti layandikira tsiku,…