Deuteronomo 21
Za wophedwa mosadziwika 1 Akapeza munthu waphedwa m’dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani likhale lanu lanu, nagona pamunda, wosadziwika wakumkantha, 2 pamenepo azituruka akuru anu ndi oweruza anu, nayese ku…
Za wophedwa mosadziwika 1 Akapeza munthu waphedwa m’dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani likhale lanu lanu, nagona pamunda, wosadziwika wakumkantha, 2 pamenepo azituruka akuru anu ndi oweruza anu, nayese ku…
Za zoweta zolowerera 1 Mukapenya ng’ombe kapena nkhosa ya mbale wako zirikusokera musamazilekerera, muzimbwezera mbale wanu ndithu. 2 Ndipo ngati mbale wanu sakhala pafupi ndi inu, kapena mukapanda kumdziwa, mubwere…
Oletsedwa ku msonkhano wa Yehova 1 Munthu wophwetekwa, wophwanyika kapena wofulika, asalowe m’msonkhano wa Yehova. 2 Mwana wa m’cigololo asalowe m’msonkhano wa Yehova, ngakhale mbadwo wace wakhumi usalowe m’msonkhano wa…
Za kalata wa cilekaniro, cikole, kuba munthu, khate 1 Munthu akatenga mkazi akhale wace, kudzali, ngati sapeza ufulu pamaso pace, popeza anapeza mwa iye kanthu kosayenera, amlembere kalata wa cilekanitso,…
Za makwapulidwe a wolakwa 1 Pakakhala ndeu pakati pa anthu, nakapita kukaweruzidwa iwowa, nakaweruza mlandu wao oweruza; azimasula wolungama, namange woipa. 2 Ndipo kudzali, wocita coipa akayenera amkwapule, woweruza amgonetse…
Copereka ca zipatso zoyamba 1 Ndipo kudzali, utakalowa m’dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani likhale colowa canu, ndipo mwacilandira ndi kukhala m’mwemo; 2 kuti muzitengako zoyamba za zipatso zonse za…
Za kuutsa miyala va cikumbutso ataoloka Yordano 1 Ndipo Mose ndi akuru a Israyeli anauza anthu, nati, Sungani malamulo onse ndikuuzani lero. 2 Ndipo kudzali, tsiku lakuoloka inu Yordano kulowa…
Madalitso pa kumvera kwao 1 Ndipo kudzali, mukadzamvera mau a Yehova Mulungu wanu mwacangu, ndi kusamalira kucita malamulo ace onse amene ndikuuzani lero, kuti Yehova Mulungu wanu adzakukulitsani koposa amitundu…
Mulungu abwereza kupangana nao 1 Awa ndi mau a cipangano cimene Yehova analamulira Mose acicite ndi ana a Israyeli m’dziko la Moabu, pamodzi ndi cipanganoco anacita nao m’Horebe. 2 Ndipo…
Mulungu alonjeza kuwalanditsa akalapa atacimwa 1 Ndipo kudzakhala, zikakugwerani zonsezi, mdalitso ndi temberero, ndinaikazi pamaso panu, ndipo mukazikumbukila mumtima mwanu mwa amitundu onse, amene Yehova Mulungu wanu anakupitikitsiraniko; 2 nimukabwerera…