Deuteronomo 11
1 Cifukwa cace muzikonda Yehova Mulungu wanu, ndi kusunga cilangizo cace, ndi malemba ace, ndi maweruzo ace, ndi malamulo ace, masiku onse. 2 Ndipo dziwani lero lino; pakuti sindinena ndi…
1 Cifukwa cace muzikonda Yehova Mulungu wanu, ndi kusunga cilangizo cace, ndi malemba ace, ndi maweruzo ace, ndi malamulo ace, masiku onse. 2 Ndipo dziwani lero lino; pakuti sindinena ndi…
Malo Oyera akhale amodzi 1 Awa ndi malemba ndi maweruzo, muziwasamalirawa kuwacita m’dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu anakupatsani likhale lanu lanu, masiku onse akukhala ndi moyo inu pa…
Acenjere nao owanyenga kuwapembedzetsa mafano 1 Akauka pakati pa inu mneneri, kapena wakulota maloto, nakakupatsani cizindikilo kapena cozizwa; 2 ndipo cizindikilo kapena cozizwa adanenaci cifika, ndi kuti, Titsate milungu yina,…
Za nyama yodyedwa ndi yosadyedwa 1 Inu ndinu ana a Yehova Mulungu wanu; musamadziceka, kapena kumeta tsitsi pakati pa maso cifukwa ca akufa. 2 Popeza ndinu mtundu wa anthu opatulikira…
Za caka ca cilekerero 1 Pakutha Pace pa zaka zisanu ndi ziwiri pakhale cilekerero. 2 Cilekereroco ndici: okongoletsa onse alekerere cokongoletsa mnansi wace; asacifunse kwa mnansi wace, kapena mbale wace;…
Madyerero a Paskha, a Masabata, ndi a Misasa 1 Samalirani mwezi wa Abibu, kuti muzicitira Yehova Mulungu wanu Paskha; popeza m’mwezi wa Abibu Yehova Mulungu wanu anakuturutsani m’dziko la Aigupto…
1 Musamaphera Yehova Mulungu wanu nsembe ya ng’ombe, kapena nkhosa, yokhala naco cirema, kapena ciri conse coipa; pakuti cinyansira Yehova Mulungu wanu. 2 Akapeza pakati panu, m’mudzi wanu wina umene…
Zoyenera ansembe ndi Alevi 1 Ansembe Alevi, pfuko lonse la Levi, alibe gawo kapena colowa pamodzi ndi Israyeli; azizidya nsembe zamoto za Yehova, ndi colowa cace, 2 Alibe colowa pakati…
Za midzi yopulumukirako 1 Pamene Yehova Mulungu wanu ataononga amitundu, amene Yehova Mulungu wanu akupatsani dziko lao, ndipo mutalilandira lanu lanu, ndi kukhala m’midzi mwao, ndi m’nyumba zao; 2 pamenepo…
Malamulo a kunkhondo 1 Pamene muturuka pa mdani wanu kunkhondo, ndi kuona akavalo ndi magareta ndi anthu akucurukira inu, musawaopa; popeza Yehova Mulungu wanu, amene anakukwezani kukuturutsani m’dziko la Aigupto,…