Cibvumbulutso 21
Miyamba yatsopano ndi dziko latsopano 1 Ndipo ndinaona m’mwamba mwatsopano ndi dziko latsopano; pakuti m’mwamba moyamba ndi dziko loyamba zidaeoka, ndipo kulibenso nyanja. 2 Ndipo ndinaona mzinda woyerawo, Yerusalemu watsopano,…
Miyamba yatsopano ndi dziko latsopano 1 Ndipo ndinaona m’mwamba mwatsopano ndi dziko latsopano; pakuti m’mwamba moyamba ndi dziko loyamba zidaeoka, ndipo kulibenso nyanja. 2 Ndipo ndinaona mzinda woyerawo, Yerusalemu watsopano,…
1 Ndipo anandionetsa mtsinje wa madzi a moyo, wonyezimira ngati krustalo, oturuka ku mpando wacifumu wa Mulungu ndi wa Mwanawarikhosa. 2 Pakati pa khwalala lace, ndi tsidya ili la mtsinje,…