Cibvumbulutso 1
Coneneratu bukuli 1 CIBVUMBULUTSO ca Yesu Kristu, cimene Mulungu anambvumbulutsira acionetsere akapolo ace, ndico ca izi ziyenera kucitika posacedwa: ndipo potuma mwa mngelo wace anazindikiritsa izi kwa kapolo wace Yohane;…
Coneneratu bukuli 1 CIBVUMBULUTSO ca Yesu Kristu, cimene Mulungu anambvumbulutsira acionetsere akapolo ace, ndico ca izi ziyenera kucitika posacedwa: ndipo potuma mwa mngelo wace anazindikiritsa izi kwa kapolo wace Yohane;…
Kalata wa kwa Mpingo wa ku Efeso 1 Kwa mngelo wa Mpingo wa ku Efeso lemba; Izi azinena iye amene agwira nyenyezi zisanu ndi ziwiri m’dzanja lace lamanja, iye amene…
Kalata wacisanu, wa kwa Mpingo wa ku Sarde 1 Ndipo kwa mngelo wa Mpingo wa ku Sarde lemba: Izi anena iye wakukhala nayo mizimu isanu ndi iwiri ya Mulungu, ndi…
Masomphenya a mpando wacifumu wa Mulungu, akuru makumi awiri ndi anai, ndi zamoyo zinai 1 Zitatha izi ndinapenya, ndipo taonani, khomo lotseguka m’Mwamba, ndipo mau oyamba ndinawamva, ngati lipenga Iakulankhuia…
Buku losindikizika ndi zosindikiza zisanu ndi ziwiri. Mwanawankhosa yekha ayenera kulitsegula 1 Ndipo ndinaona m’dzanja lamanja la iye wakukhala pa mpando wacifumu buku lolembedwa m’kati ndi kunja kwace, losindikizika ndi…
Atsegula zosindikiza zisanu ndi cimodzi 1 Ndipo ndinaona pamene Mwanawankhosa anamasula cimodzi ca zizindikilo zisanu ndi ziwiri, ndipo ndinamva cimodzi mwa zamoyo zinai, nicinena, ngati mau a bingu, Idza. 2…
Aisrayeli okhulupirika alanditsidwa 1 Zitatha izi ndinao na angelo anai alinkuimirira pa ngondya zinai za dziko, akugwira mphepo zinai za dziko, kuti ingaombe mphepo padziko, kapena panyanja, kapena pa mtengo…
Atsegula cosindikiza cacisanu ndi ciwiri. Angelo asanu ndi awiri, ndi malipenga oyamba anai 1 Ndipo pamene anamasula cizindikilo cacisanu ndi ciwiri, munali cete m’Mwamba monga mwa nthawi ya ora latheka….
Lipenga lacisanu, tsoka loyamba 1 Ndipo mngelo wacisanu anaomba, ndipo ndinaona nyenyezi yocokera kumwamba idagwa padziko; ndipo anampatsa iye cifunguliro ca dzenje la phompho. 2 Ndipo anatsegula pa dzenje la…
Yohane adya buku locokera Kumwamba 1 Ndipo ndinaona mngelo wina wolimba alikutsika Kumwamba, wobvala mtambo; ndi utawaleza pamutu pace, ndi nkhope yace ngati dzuwa, ndi mapazi ace ngati mizati yamoto;…