Aroma 1
1 PAULO, kapolowa Yesu Kristu, mtumwi woitanidwa, wopatulidwa kukanena Uthenga Wabwino wa Mulungu, 2 umene iye analonjeza kale ndi mau a ananeri ace m’malembo oyera, 3 wakunena za Mwana wace,…
1 PAULO, kapolowa Yesu Kristu, mtumwi woitanidwa, wopatulidwa kukanena Uthenga Wabwino wa Mulungu, 2 umene iye analonjeza kale ndi mau a ananeri ace m’malembo oyera, 3 wakunena za Mwana wace,…
Kusamvera kwa Ayuda 1 Cifukwa cace uli wopanda mau owiringula, munthu iwe, amene uli yense wakuweruza; pakuti m’mene uweruza wina, momwemo udzitsutsa iwe wekha, pakuti iwe wakuweruza, umacita zomwezo. 2…
Kuposa kwace kwa Myuda Mulungu ali wolungama 1 Ndipo potero Myuda aposa Dinji? Kapena mdulidwe upindulanji? 2 Zambiri monse monse: coyamba, kuti mau a Mulungu anaperekedwa kwa iwo. 3 Nanga…
Abrahamu anayesedwa wolungama ndi cikhulupiriro 1 Ndipo tsono tidzanena kuti Abrahamu, kholo lathu monga mwa thupi, analandira ciani? 2 Pakuti ngati Abrahamu anayesedwa wolungama cifukwa ca nchito, iye akhala naco…
Zipatso za Cikhulupiriro 1 Popeza tsono tayesedwa olungama ndi cikhulupiriro, tikhala ndi mtendere ndi Mulungu mwa Ambuye wathu Yesu Kristu; 2 amene ife tikhoza kulowa naye ndi cikhulupiriro m’cisomo ici…
Kristu anatityolera mphamvu ya zotpa 1 Cifukwa cace tidzatani? Tidzakhalabe m’ucimo kodi, kuti cisomo cicuruke? 2 Msatero ai. Ife amene tiri akufa ku ucimo, tidzakhala bwanji cikhalire m’menemo? 3 Kapena…
Okhulupirira akwatiwa ndi Kristu 1 Nanga kodi simudziwa, abale, pakuti ndilankhula ndi anthu akudziwa lamulo, kuti lamulolo licita ufumu pa munthu nthawi zonse iye ali wamoyo? 2 Pakuti mkazi wokwatidwa…
Mayo watha watsopano mwa Kristu 1 Cifukwa cace tsopano iwo akukhala mwa Kristu Yesu alibe kutsutsidwa. 2 Pakuti cilamulo ca mzimu wa moyo mwa Kristu Yesu candimasula ine ku lamulo…
Paulo alirira kusamvera kwa Israyeli 1 Ndinena zoona mwa Kristu, sindinama ai, cikumbu mtima canga cicita umboni pamodzi ndine mwa Mzimu Woyera, 2 kuti ndagwidwa ndi cisoni cacikuru ndi kuphwetekwa…
Ayuda anataya cilungamo ca Mulungu 1 Abale, kufunitsa kwa mtima wanga ndi pemphero langa limene ndiwapempherera kwa Mulungu, ndilo, kuti apulumuke. 2 Pakuti ndiwacitira iwo umboni kuti a ali ndi…