Ahebri 11
Mtima wa cikhulupiriro. Okhulupirira a m’Cipangano cakale 1 Koma cikhulupiriro ndico cikhazikitso ca zinthu zoyembekezeka, ciyesero ca zinthu zosapenyeka. 2 Pakuti momwemo akulu anacitidwa umboru. 3 Ndi cikhulupiriro tizindikira kuti…
Mtima wa cikhulupiriro. Okhulupirira a m’Cipangano cakale 1 Koma cikhulupiriro ndico cikhazikitso ca zinthu zoyembekezeka, ciyesero ca zinthu zosapenyeka. 2 Pakuti momwemo akulu anacitidwa umboru. 3 Ndi cikhulupiriro tizindikira kuti…
Tipirire angakhale masautso acuruka, monga anatero Kristu 1 Cifukwa cace ifenso, popeza tizingidwa nao mtambo waukuru wotere wa mboni, titaye colemetsa ciri conse, ndi cimoli Iimangotizinga, ndipo tithamange mwacipiriro makaniwo…
1 Cikondi ca pa abale cikhalebe. 2 Musaiwale kucereza alendo; pakuti mwa ici ena anacereza angelo osacidziwa. 3 Kumbukilani am’nsinga, monga am’nsinga anzao; ocitidwa zoipa, monga ngati inunso adatero nanu…