Ahebri 1
Kristu Mwana wa Mulungu aposatu angelo 1 KALE Mulungu analankhula ndi makolo mwa aneneri m’manenedwe ambiri ndi mosiyana-siyana, 2 koma pakutha pace pa masiku ano analankhula ndi ife ndi Mwana…
Kristu Mwana wa Mulungu aposatu angelo 1 KALE Mulungu analankhula ndi makolo mwa aneneri m’manenedwe ambiri ndi mosiyana-siyana, 2 koma pakutha pace pa masiku ano analankhula ndi ife ndi Mwana…
Yesu Kristu Nkhoswe yathu yakuposa angelo akhoza kumva nate cifundo 1 Mwa ici tiyenera kusamaliradi zimene tidazimvazi kuti kapena tingatengedwe ndi kusiyana nazo. 2 Pakuti ngati mau adalankhulidwa ndi angelo…
Kristu ali wamkuru woposa Mose, Awacenjeza amkhulupirire 1 Potero, abale oyera mtima, olandirana nao maitanidwe akumwamba, lingirirani za Mtumwi ndi. Mkuluwansembe wa cibvomerezo cathu, Yesu; 2 amene anakhala wokhulupirika kwa…
1 Cifukwa cace tiope kuti kapena likatsala lonjezano lakulowa mpumulo wace, wina wa inu angaoneke ngati adaliperewera. 2 Pakuti kwa ifenso walalikidwa Uthenga Wabwino, monganso kwa iwo; koma iwowa sanapindula…
1 Pakuti mkulu wa ansembe ali yense, wotengedwa mwa anthu, amaikika cifukwa ca anthu m’zinthu za kwa Mulungu, kuti apereke mitulo, ndiponso nsembe, cifukwa ca macimo: 2 akhale wokhoza kumva…
1 Mwa ici, polekana nao mau a ciyambidwe ca Kristu, tipitirire kutsata ukulu msinkhu; osaikanso maziko a kutembenuka mtima kusiyana nazo nchito zakufa, ndi a cikhulupiriro ca pa Mulungu, 2…
Mkuru wa ansembe Melikizedeke afanizira Yesu Kristu, Mkuruwansembe wosatha 1 Pakuti Melikizedeke uyu, Mfumu ya Salemu, wansembe wa Mulungu Wamkulukulu, amene anakomana ndi Abrahamu, pobwera iye adawapha mafumu aja, namdalitsa,…
Cipangano cakale ndi cofanizira ndi copita, Kristu ali Nkhoswe ya cipangano cosatha 1 Koma mutu wafzi tanenazi ndi uwu: Tiri naye Mkuruwansembe wotere, amene anakhala pa dzanja lamanja la mpando…
Nsembe za’cipangano cakale zidacitika kawiri kawiri, nsembe ya Yesu idacitika kamodzi kokha 1 Ndipo cingakhale cipangano coyambaci cinali nazo zoikika za kulambira, ndi malo opatulika a pa dziko lapansi. 2…
Pakuti cilamulo pokhala nao 1 mthunzi wa zokoma zirinkudza, osati cifaniziro ceni ceni ca zinthuzo, sicikhozatu, ndi nsembe zomwezi caka ndi caka, zimene azipereka kosalekeza, kuwayesera angwiro iwo akuyandikira. 2…