2 Samueli 1
Amuuza Davide za imfa ya Sauli 1 NDIPO kunali atamwalira Sauli, pamene Davide anabwera atawapha Aamaleki, ndipo Davide atakhala ku Zikilaga masiku awiri; 2 pa tsiku lacitatu, onani, munthu anaturuka…
Amuuza Davide za imfa ya Sauli 1 NDIPO kunali atamwalira Sauli, pamene Davide anabwera atawapha Aamaleki, ndipo Davide atakhala ku Zikilaga masiku awiri; 2 pa tsiku lacitatu, onani, munthu anaturuka…
Davide alowa ufumu wa Yuda 1 Ndipo zitatha izi Davide anafunsira kwa Yehova nati, Kodi ndikwere kunka m’mudzi wina wa Yuda? Ndipo Yehova ananena naye, Kwera. Davide nanena naye, Ndikwere…
1 Ndipo panali nkhondo nthawi yaitali pakati pa nyumba ya Sauli ndi nyumba ya Davide. Koma Davide analimba cilimbire, ndi nyumba ya Sauli inafoka cifokere. Ana obadwira Davide ku Hebroni…
Isiboseti aphedwa, Davide alanga omupha 1 Ndipo pamene Isiboseti mwana wa Sauli, anamva kuti Abineri adakafera ku Hebroni, manja ace anafoka, ndi Aisrayeli onse anabvutika. 2 Ndipo Isiboseti, mwana wa…
Mafuko onse abvomereza Davide mfumu yao 1 Pomwepo mafuko onse a Israyeli anabwera kwa Davide ku Hebroni, nalankhula nati, Taonani, ife ndife pfupa lanu ndi mnofu wanu. 2 Masiku anapitawo,…
Atenga likasa la Mulungu ku nyumba ya Abinadabu 1 Pambuyo pace Davide anamemezanso osankhika onse a m’Israyeli, anthu zikwi makumiatatu. 2 Ndipo Davide ananyamuka, namuka nao anthu onse anali naye,…
Mulungu salola Davide ammangire nyumba 1 Ndipo kunali pakukhala mfumuyo m’nyumba mwace, atampumulitsa Yehova pa adani ace onse omzungulira, 2 mfumuyo inanena ndi Natani mneneriyo, Onani ndirikukhala ine m’nyumba yamikungudza,…
Davide agonjetsa amitundu ena 1 Ndipo m’tsogolo mwace Davide anakantha Afilisti, nawagonjetsa; Davide nalanda mudzi wa Metege Ama m’manja mwa Afilisti. 2 Ndipo anakantha Amoabu nawayesa ndi cingwe, nawagonetsa pansi;…
Davide acitira Mefiboseti mwana wa Jonatani cifundo 1 Ndipo Davide anati, Kodi atsalako wina wa nyumba ya Sauli, kuti ndimcitire cifundo cifukwa ca Jonatani? 2 Ndipo panali mnyamata wa m’nyumba…
Davide akantha Aamoni ndi Aaramu 1 Ndipo kunali zitapita izi, mfumu ya ana a Amoni inamwalira, ndipo Hanuni mwana wace anakhala mfumu m’malo mwace. 2 Ndipo Davide anati, Ndidzacitira Hanuni…