2 Petro 1
1 SIMONI Petro, kapolo ndi mtumwi wa Yesu Kristu kwa iwo amene adalandira cikhulupiriro ca mtengo wace womwewo ndi ife, m’cilungamo ca Mulungu wathu ndi Mpulumutsi Yesu Kristu: 2 Cisomo…
1 SIMONI Petro, kapolo ndi mtumwi wa Yesu Kristu kwa iwo amene adalandira cikhulupiriro ca mtengo wace womwewo ndi ife, m’cilungamo ca Mulungu wathu ndi Mpulumutsi Yesu Kristu: 2 Cisomo…
Za aphunzitsi onyenga 1 Koma padakhalanso pakati pa anthuwo aneneri onama, monganso padzakhala aphunzitsi onama pakati pa inu, amene adzalowa nayo m’tseri mipatuko yotayikitsa, nadzakana Ambuye amene adawagula, nadzadzitengera iwo…
Kubwera kwa Ambuye 1 Okondedwa, uyu ndiye kalata waciwiri ndilembera kwa inu tsopano; mwa onse awiri nditsitsimutsa mtima wanu woona ndi kukukumbutsani; 2 kuti mukumbukile mau onenedwa kale ndi aneneri…