2 Mbiri 11
Mulungu aletsa nkhondo pakati pa Yuda ndi Israyeli 1 Ndipo atafika ku Yerusalemu Rehabiamu, anamemeza a nyumba ya Yuda ndi Benjamini amuna osankhika zikwi zana limodzi mphambu makumi asanu ndi…
Mulungu aletsa nkhondo pakati pa Yuda ndi Israyeli 1 Ndipo atafika ku Yerusalemu Rehabiamu, anamemeza a nyumba ya Yuda ndi Benjamini amuna osankhika zikwi zana limodzi mphambu makumi asanu ndi…
Sisaki wa ku Aigupto athira nkhondo Rehabiamu 1 Ndipo kunacitika, utakhazikika ufumu wa Rehabiamu, nalimbika iye, anasiya cilamulo ca Yehova, ndi Aisrayeli onse pamodzi naye. 2 Ndipo Rehabiamu atakhala mfumu…
Abiya ndi Yerobiamu agwirana nkhondo, Israyeli akanthidwa 1 Ndipo caka cakhumi mphambu zisanu ndi zitatu ca Yerobiamu, Abiya analowa ufumu wa Yuda. 2 Anakhala mfumu m’Yerusalemu zaka zitatu; ndi dzina…
Asa akantha Akusi 1 Momwemo Abiya anagona ndi makolo ace, ndipo anamuika m’mudzi wa Davide; ndi Asa mwana wace anakhala mfumu m’malo mwace, m’masiku ace dziko linaona bata zaka khumi….
Asa acotsa mafano nabwereza cipangano ndi Mulungu 1 Pamenepo mzimu wa Mulungu unagwera Azariya mwana wa Odedi, 2 ndipo anaturuka kukomana naye Asa, nanena naye, Mundimvere, Asa, ndi onse Ayuda…
Asa apangana ndi Benihadadi, nalimbana ndi Israyeli 1 Caka ca makumi atatu mphambu zisanu ndi cimodzi ca Asa, Basa mfumu ya Israyeli anakwera kulimbana ndi Yuda, namangitsa Rama, kuwaletsa anthu…
Ukoma ndi ukulu wa Yehosafati 1 Ndipo Yehosafati mwana wace anakhala mfumu m’malo mwace, nadzilimbitsa kuyambana ndi Israyeli. 2 Naika ankhondo m’midzi yonse yamalinga ya Yuda, naika aboma m’dziko la…
Pangano pakati pa Yehosafati ndi Ahabu; afunsira kwa aneneri 1 Yehosafati tsono anali nacocuma ndi ulemu zomcurukira, nacita cibale ndi Ahabu. 2 Ndipo zitatha zaka zina, anatsikira kwa Ahabu ku…
Mneneri Yehu adzudzula Yehosafati 1 Ndipo Yehosafati mfumu ya Yuda anabwerera ku nyumba yace ku Yerusalemu mumtendere. 2 Naturuka Yehu mwana wa Hanani mlauli kukomana naye, nati kwa mfumu Yehosafati,…
Yehosafati apempha Yehova pa Amoabu ndi Aamoni 1 Ndipo zitatha izi, kunacitika kuti ana a Moabu, ndi ana a Amoni, ndi ena pamodzi ndi Aamoni, anadza kuyambana nkhondo ndi Yehosafati….