2 Mbiri 1
Solomo apereka nsembe ku Gibeoni 1 NDIPO Solomo mwana wa Davide analimbikitsidwa m’ufumu wace, ndipo Yehova Mulungu wace anali naye, namkuza kwakukuru. 2 Ndipo Solomo analankhula ndi Aisrayeli onse, ndi…
Solomo apereka nsembe ku Gibeoni 1 NDIPO Solomo mwana wa Davide analimbikitsidwa m’ufumu wace, ndipo Yehova Mulungu wace anali naye, namkuza kwakukuru. 2 Ndipo Solomo analankhula ndi Aisrayeli onse, ndi…
Solomo apangana ndi Hiramu za mirimo ya Kacisi 1 Ndipo a Solomo anati alimangire dzina la Yehova nyumba, ndiponso nyumba ya ufumu wace. 2 Nawerenga Solomo amuna zikwi khumi mphambu…
Mamangidwe a Kacisi 1 Pamenepo Solomo anayamba kumanga nyumba ya Yehova ku Yerusalemu, m’phiri la Moriya, kumene Mulungu anaonekera kwa Davide atate wace, pamalo pamene Davide anakonzeratu pa dwale la…
Guwa la nsembe ndi thawale lamkawa ndi zipangizo zonse zina 1 Anapanganso guwa la nsembe lamkuwa, m’litali mwace mikono makumi awiri, ndi kupingasa kwace mikono makumi awiri, ndi msinkhu wace…
1 Momwemo zidatha nchito zonse Solomo adazicitira nyumba ya Yehova. Ndipo Solomo anabwera nazo zopatulika zija za atate wace Davide; naziika siliva, ndi golidi, ndi zipangizo zonse m’cuma ca nyumba…
Conena Solomo ndi pemphero lace popereka Kacisi 1 Pamenepo Solomo anati, Yehova anati kuti adzakhala mu mdima wandiweyani. 2 Koma ndakumangirani nyumba yokhalamo, malo okhazikika okhalamo Inu nthawi yosatha. 3…
Cibvomerezo ca Yehova mwa moto ndi ulemerero wao wodzaza Kacisi 1 Atatha tsono Solomo kupemphera, moto unatsika kumwamba, nunyeketsa nsembe yopsereza, ndi nsembe zophera; ndipo ulemerero wa Yehova unadzaza nyumbayi….
Solomo amanga midzi yina 1 Ndipo kunali, zitatha zaka makumi awiri m’mene anamanga nyumba ya Yehova, ndi nyumba yace yace, 2 Solomo anamanga midzi imene Huramu adampatsa, nakhalitsamo ana a…
Mfumu yaikazi ya ku Seba aceza ndi Solomo 1 Ndipo atamva mfumu yaikazi ya ku Seba mbiri ya Solomo, anadza kumuyesera Solomo ndi miyambi yododometsa ku Yerusalemu, ndi ulendo waukuru,…
Ufumu ugawanika pakati. Rehabiamu mfumu ya Yuda, Yerobiamu ya Israyeli 1 Ndipo Rehabiamu anamuka ku Sekemu; pakuti Aisrayeli onse adadza ku Sekemu kumlonga ufumu. 2 Ndipo kunali, atamva Yerobiamu mwana…