2 Mafumu 11
A taliya aononga mbumba yacifumu ya Yuda; apulumuka Yoasi, aphedwa Ataliya 1 Pamene Ataliya mace wa Ahaziya anaona kuti mwana wace wafa, ananyamuka, naononga mbeu yonse yacifumu. 2 Koma Yoseba…
A taliya aononga mbumba yacifumu ya Yuda; apulumuka Yoasi, aphedwa Ataliya 1 Pamene Ataliya mace wa Ahaziya anaona kuti mwana wace wafa, ananyamuka, naononga mbeu yonse yacifumu. 2 Koma Yoseba…
Yoasi akonza Kacisi 1 Caka cacisanu ndi ciwiri ca Yehu, Yoasi analowa ufumu wace; nakhala mfumu m’Yerusalemu zaka makumi anai; ndi dzina la mai wace ndiye Zibiya wa ku Beereseba….
Yoahazi mfumu ya Israyeli 1 Caka ca makumi awiri ndi zitatu ca Yoasi mwana wa Ahaziya mfumu ya Yuda, Yoahazimwana wa Yehu analowa ufumu wace wa Israyeli ku Samariya, nakhala…
Amaziyamfumu ya Yuda, Yoasi ndi Yerobiamu waciwiri mafumu a Israyeli 1 Caka caciwiri ca Yoasi mwana wa Yoahazi mfumu ya Israyeli, Amaziya mwana wa Yoasi mfumu ya Yuda analowa ufumu…
Azariya mfumu ya Yuda 1 Caka ca makumi awiri mphambu zisanu ndi ziwiri ca Yerobiamu mfumu ya Israyeli, Azariya mwana wa Amaziya mfumu ya Yuda analowa ufumu wace. 2 Anali…
Ahazi mfumu ya Yuda 1 Caka cakhumi mphambu zisanu ndi ziwiri ca Peka mwana wa Remaliya Ahazi mwana wa Yotamu mfumu ya Yuda analowa ufumu wace. 2 Ahazi anali wa…
Hoseyamfumu yotsiriza ya Israyeli, Salimanezeri mfumu ya Asuri apasula Samariya, Aisrayeli natengedwa ukapolo 1 Caka cakhumi ndi ziwiri ca Ahazi mfumu ya Yuda Hoseya mwana wa Ela analowa ufumu wace…
Hezekiya wabwino akhazikanso cipembedzo ca Yehova 1 Ndipo kunali caka cacitatu ca Hoseya mwana wa Ela mfumu ya Israyeli, Hezekiya mwana wa Ahazi mfumu ya Yuda analowa ufumu waceo 2…
Nkhawa ya Hezekiya ndi pemphero lace 1 Ndipo kunali, atamva Hezekiya, anang’amba zobvala zace, napfundira ciguduli, nalowa m’nyumba ya Yehova. 2 Natuma Eliyakimu woyang’anira nyumbayo, ndi Sebina mlembi, ndi akuru…
Hezekiya adwala nacira 1 Masiku ajawo Hezekiya anadwala, nafuna kufa. Namdzera Yesaya mneneri mwana wa Amozi, nanena naye, Atero Yehova, Siyira banja lako; pakuti udzafa, sudzakhala ndi moyo. 2 Pamenepo…