1 Yohane 1
Mau a moyo aoneka m’thupi 1 CIMENE cinaliko kuyambira paciyambi, cimene tidacimva, cimene tidaciona m’maso mwathu, cimene tidacipenyerera, ndipo manja athu adacigwira ca Mau a moyo, 2 (ndipo moyowo unaonekera,…
Mau a moyo aoneka m’thupi 1 CIMENE cinaliko kuyambira paciyambi, cimene tidacimva, cimene tidaciona m’maso mwathu, cimene tidacipenyerera, ndipo manja athu adacigwira ca Mau a moyo, 2 (ndipo moyowo unaonekera,…
1 Tiana tanga, izi ndikulemberani, kuti musacimwe. Ndipo akacimwa wina, Nkhoswe tiri naye kwa Atate, ndiye Yesu Kristu wolungama; 2 ndipo iye ndiye ciombolo ca macimo athu; koma wosati athu…
Ife ndife ana a Mulungu 1 Taonani, cikondico Atate watipatsa, kuti tichedwe ana a Mulungu; ndipo tiri ife otere. Mwa ici dziko lapansi silizindikira ife, popeza silimzindikira iye. 2 Okondedwa,…
Za aphunzitsi onyenga 1 Okondedwa, musamakhulupirira mzimu uli wonse, koma yesani mizimu ngati icokera mwa Mulungu: popeza aneneri onyenga ambiri anaturuka kulowa m’dziko lapansi. 2 M’menemo muzindikira Mzimu Wl Mulungu:…
Za kukhulupirira Yesu ndi zotsatira zace 1 Yense wokhulupirira kuti Yesu ndiye Kristu wabadwa kucokera kwa Mulungu; ndipo yense wakukonda iye amene anabala akondanso iye amene anabadwa wocokera mwa iye….