1 Samueli 21

Davide athawira kwa wansembe Ahimeleki ku Nobi 1 Ndipo Davide anafika ku Nobi kwa! Ahimeleki wansembeyo; ndipo Ahimeleki anadza kukomana ndi Davide alikunjenjemera, nanena naye, Muli nokha bwanji, palibe munthu…

1 Samueli 22

Davide apulumukira ku phanga La Adulamu 1 Motero Davide anacoka kumeneko, napulumukira ku phanga la ku Adulamu; ndipo pamene abale ace ndi banja lonse la atate wace anamva, iwo anatsikira…

1 Samueli 23

Davide alanditsa a ku Keila 1 Tsono anauza Davide, kuti, Onani Afilisti alikuponyana ndi Keila, nafunkha za m’madwale. 2 Cifukwa cace Davide anafunsira kwa Yehova, nati, Ndimuke kodi kukakantha Afilisti…

1 Samueli 24

Davide aleka Sauli osamupha 1 Ndipo kunali, pakubwerera Sauli potsata Afilisti, anamuuza, kuti, Taonani, Davide ali ku cipululu ca Engedi. 2 Tsono Sauli anatenga anthu zikwi zitatu osankhika pakati pa…

1 Samueli 25

Amwalira Samueli 1 Ndipo Samueli anamwalira; ndi Aisrayeli onse anaunjikana pamodzi nalira maliro ace, namuika m’nyumba yace ku Rama. Davide nanyamuka, natsikira ku cipululu ca Parana. Za Davide, Nabala ndi…

1 Samueli 26

Davide alekanso Sauli osamupha 1 Ndipo Azifi anafika kwa Sauli ku Gibeya, nati, Kodi Davide sali kubisala m’phiri la Hagila, kupenya kucipululu! 2 Ndipo Sauli ananyamuka, natsikira ku cipululu ca…

1 Samueli 27

1 Ndipo Davide ananena mumtima mwace, Tsiku tina Sauli adzandipha; palibe cina condikomera koma kuti ndithawire ku dziko la Afilisti; ndipo Sauli adzakhala kakasi cifukwa ca ine, osandifunanso m’malire onse…

1 Samueli 28

Sauli afunsira mkazi wobwebweta ku Endori 1 Ndipo kunali masiku aja, Afilisti anasonkhanitsa pamodzi makamu ao onse kunkhondo, kuti akaponyane ndi Aisrayeli. Ndipo Akisi ananena ndi Davide, Dziwa kuti zoonadi,…

1 Samueli 29

Afilisti abweza Davide kunkhondo 1 Tsono Afilisti anasonkhanitsa makamu ao onse ku Afeki; ndipo Aisrayeli anamanga ku citsime ca m’Jezreeli. 2 Ndipo akalonga a Afilisti ananyamuka ndi mazana ao ndi…

1 Samueli 30

Davide alanditsa a ku Zikilaga m’manja mwa Aamaleki 1 Ndipo kunali, pakufika Davide ndi anthu ace ku Zikilaga tsiku lacitatu, Aamaleki adaponya nkhondo yobvumbulukira kumwera, ndi ku Zikilaga, nathyola Zikilaga…