1 Samueli 1
1 NDIPO panali munthu wina wa ku Ramatayimu Zofimu, wa dziko la mapiri la Efraimu, dzina lace ndiye Elikana, mwana wace wa Yerohamu, mwana wa Elihu, mwana wa Tohu, mwana…
1 NDIPO panali munthu wina wa ku Ramatayimu Zofimu, wa dziko la mapiri la Efraimu, dzina lace ndiye Elikana, mwana wace wa Yerohamu, mwana wa Elihu, mwana wa Tohu, mwana…
Coyamikira ca Hana 1 Ndipo Hana anapemphera, nati Mtima wanga umyuka mokondwera kwa Yehova, Nyanga yanga yakwezeka mwa Yehova; Pakamwa panga pakula kwa adani anga; Popeza ndikondwera m’cipulumutsocanu. 2 Palibe…
Masomphenya a Samueli 1 Ndipo mwanayo Samueli anatumikira Yehova pamaso pa Eli. Ndipo masiku aja mau a Yehova anamveka kamodzi kamodzi; masomphenya sanaoneka-oneka. 2 Ndipo kunali nthawi yomweyo Eli atagona…
Afilisti akantha Aisrayeli 1 Ndipo mau a Samueli anafikira kwa Aisrayeli onse. Ndipo Aisrayeli anaturuka kukaponyana nkhondo ndi Afilisti, namanga zithando zao ku Ebenezeri; Afilistiwo namanga m’Afeki. 2 Ndipo Afilistiwo…
Likasa la Mulungu ku nyumba ya Dagoni 1 Ndipo Afilisti anatenga likasa la Mulungu, nacoka nalo ku Ebenezeri, napita ku Asidodi. 2 Ndipo Afilistiwo anatenga likasa la Mulungu, nafika nalo…
Afilisti abweza likasa ku dziko la Aisrayeli 1 Ndipo likasa la Yehova linakhala ku dziko la Afilisti miyezi isanu ndi iwiri. 2 Ndipo Afilistiwo anaitana ansembe ndi oombeza, nati, Ticitenji…
1 Ndipo anthu a ku Kiriati-yearimu anabwera, natenga likasa la Yehova, nafika nalo m’nyumba ya Abinadabu paphiri; napatula mwana wace wamwamuna Eleazeri kuti asunge likasa la Yehova. Afilisti akanthidwa ku…
Aisrayeli akhumba mfumu 1 Ndipo kunali, pamene Samueli anakalamba, anaika ana ace amuna akhale oweruza a Israyeli. 2 Dzina la mwana wace woyamba ndiye Yoeli, ndi dzina la waciwiri ndiye…
Sauli afuna aburu olowerera a atate wace 1 Ndipo panali munthu Mbenlamlni, dzina lace ndiye Kisi, mwana wa Abiyeli, mwana wa Zerori, mwana wa Bekorati, mwana wa Afiya, mwana wa…
Samueli; adzoza Sauli akhale mfumu ya Israyeli 1 Pamenepo Samueli anatenga nsupa ya mafuta, nawatsanulira pamutu pace, nampsompsona iye, nati, Sanakudzozani ndi Mulungu kodi, mukhale mfumu ya pa colowa cace?…