1 Petro 1
1 PETRO, mtumwi wa Yesu Kristu, kwa osankhidwa akukhala: alendo a cibalaliko a ku Ponto, Galatiya, Kapadokiya, Asiya, ndi Bituniya, 2 monga mwa kudziwiratu kwa Mulungu Atate, m’ciyeretso ca Mzimu,…
1 PETRO, mtumwi wa Yesu Kristu, kwa osankhidwa akukhala: alendo a cibalaliko a ku Ponto, Galatiya, Kapadokiya, Asiya, ndi Bituniya, 2 monga mwa kudziwiratu kwa Mulungu Atate, m’ciyeretso ca Mzimu,…
1 Momwemo pakutaya coipa conse, ndi cmyengo conse, ndi maonekedwe onyenga, ndi kadoka, ndi masiniiriro onse, 2 lirani monga makanda alero mkaka woyenera, wopanda cinyengo, kuti mukakule nao kufikira cipulumutso;…
Zoyenera akazi ndi amuna 1 Momwemonso, akazi inu, mverani amuna anu ainu nokha; kuti, ngatinso ena samvera mau, akakodwe opanda mau mwa mayendedwe a akazi; 2 pakuona mayendedwe anu oyera…
1 Popeza Kristu adamva zowawa m’thupi, mudzikonzere mtima womwewo; pakuti iye amene adamva zowawa m’thupi walekana nalo cimo; 2 kuti nthawi yotsalira simukakhalenso ndi moyo m’thupi kutsata zilakolako za anthu,…
Zoyenera akulu ndi anyamata; adzicepetse, adikire 1 Akulu tsono mwa inu ndiwadandaulira, ine mkulu mnzanu ndi mboni ya zowawa za Kristu, ndinenso wolawana nao ulemerero udzabvumbulutsikawo: 2 Wetani gulu la…