1 Mbiri 1
Maina a makolo kuyambira Adamu kufikira adzukulu a Nowa 1 ADAMU, Seti, Enosi, 2 Kenani, Mahalaheli, Yaredi, 3 Enoki, Metusela, Lameki, 4 Nowa, Semu, Hamu, ndi Yafeti. 5 Ana a…
Maina a makolo kuyambira Adamu kufikira adzukulu a Nowa 1 ADAMU, Seti, Enosi, 2 Kenani, Mahalaheli, Yaredi, 3 Enoki, Metusela, Lameki, 4 Nowa, Semu, Hamu, ndi Yafeti. 5 Ana a…
Ana a Israyeli, adzukulu a Yuda 1 Ana a Israyeli ndi awa: Rubeni, Simeoni, Levi, ndi Yuda, Isakara, ndi Zebuluni, 2 Dani, Yosefe, ndi Benjamini, Nafitali, Gadi, ndi Aseri. 3…
Adzukulu a Davide 1 Ana Davide tsono ombadwira ku Hebroni: woyamba a Amnoni wa Ahinoamu wa ku Yezreeli, waciwiri Danieli wa Abigaili wa ku Karimeli, 2 wacitatu Abisalomu mwana wa…
Adzukulu a Yuda 1 Ana a Yuda: Perezi, Hezroni, ndi Karmi, ndi Huri, ndi Sobala. 2 Ndipo Reaya mwana wa Sobala anabala Yahati; ndi Yahati anabala Ahumai, ndi Lahadi. Iwo…
Adzukulu a Rubeni 1 Ndipo ana a Rubeni mwana woyamba wa Israyeli, (pakuti ndiye mwana woyamba; koma popeza anaipsa kama wa atate wace ukulu wace unapatsidwa kwa ana a Yosefe…
Adzukulu a Levi 1 Ana a Levi: Gerisomu, Kohati, ndi Merari. 2 Ndi ana a Kohati: Amramu, Izara, ndi Hebroni, ndi Uzieli. 3 Ndi ana a Amramu: Aroni, ndi Mose,…
Adzukulu a Isakara 1 Ana a Isakara ndiwo Tola, ndi Pua, Yasubu ndi Simironi; anai. 2 Ndi ana a Tola: Uzi, ndi Repaya, ndi Yerieli, ndi Yamai, ndi Ibsamu, ndi…
Adzukulu a Benjamini ndi Sauli 1 Ndipo Benjamini anabala Bela mwana wace vyoyamba, Asibeli waciwiri, ndi Ahara wacitatu, 2 Noha wacinai, ndi Rafa wacisanu. 3 Ndi Bela anali ndi ana:…
Okhala m’Yerusalemu atabwera kucokera ku Babulo 1 Ndipo Aisrayeli onse anawerengedwa mwa cibadwidwe cao; ndipo taonani, alembedwa m’buku la mafumu a Israyeli; ndipo Yuda anatengedwa ndende kumka ku Babulo cifukwa…
Za imfa ya Sauli ndi ana ace 1 Afilisti tsono analimbana nkhondo ndi Israyeli; ndipo amuna a Israyeli anathawa pamaso pa Afilisti, nagwa ophedwa pa phiri la Giliboa. 2 Ndipo…