1 Mafumu 1

Ukalamba wa Davide, achula Saloma wodzalowa m’malo mwace 1 NDIPO mfumu Davide anakalamba nacuruka masiku ace; ndipo iwo anampfunda ndi zopfunda, koma iye sanafundidwa. 2 Pamenepo anyamata ace ananena naye,…

1 Mafumu 2

Davide atapangira Solomo amwalira 1 Pakuyandikira masiku ace a Davide akuti amwalire, analamulira Solomo mwana wace, nati, 2 Ndimuka ine njira ya dziko lonse: limba mtima tsono, nudzionetse umunthu; 3…

1 Mafumu 3

Solomo akwatira mwana wa Farao 1 Ndipo Solomo anapalana ubwenzi ndi Farao mfumu ya Aigupto, natenga mwana wamkazi wa Farao, nadza naye ku mudzi wa Davide, mpaka atamanga nyumba ya…

1 Mafumu 4

Nduna za Solomo, ukuru wa ufumu wace 1 Ndipo mfumu Solomo anali mfumu ya Israyeli yense. 2 Ndipo akuru a mfumu ndi awa: Azariya mwana wa Zadoki anali nduna, 3…

1 Mafumu 5

Solomo apangana ndi Hiramu za mirimo vomansa nayo Kacisi 1 Ndipo Hiramu mfumu ya ku Turo anatuma anyamata ace kwa Solomo, popeza anamva kuti adamdzoza mfumu m’malo mwa atate wace;…

1 Mafumu 6

Za mamangidwe a Kacisi 1 Ndipo kunacitika zitapita zaka mazana anai mphambu makumi asanu ndi atatu ataturuka ana a Israyeli m’dziko la Aigupto, caka cacinai cakukhala Solomo mfumu ya Israyeli,…

1 Mafumu 7

Mamangidwe a nyumba Yd Solomo 1 Koma nyumba ya iye yekha Solomo anaimanga zaka khumi mphambu zitatu, natsiriza nyumba yace yonse. 2 Anamanganso nyumba yochedwa Nkhalango ya Lebano, m’litali mwace…

1 Mafumu 8

Aika likasa m’Kacisi 1 Pamenepo Solomo anasonkhanitsa akulu a Israyeli, ndi akulu onse a mafuko, akalonga a nyumba za atate a ana a Israyeli, kwa mfumu Solomo m’Yerusalemu, kukatenga likasa…

1 Mafumu 9

Mulungu aonekanso kwa Solomo 1 Ndipo kunali, atatsiriza Solomo kumanga nyumba ya Yehova, ndi nyumba ya mfumu, ndi cifuniro conse ca Solomo anacikhumbaco, 2 Yehova anaonekera kwa Solomo nthawi yaciwiri,…

1 Mafumu 10

Mfumu yaikazi ya ku Seba adzaceza kwa Solomo ku Yerusalemu 1 Ndipo atamva mfumu yaikazi ya ku Seba mbiri ya Solomo yakubukitsa dzina la Yehova, anadza kumuyesera iye ndi miyambi…